Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 41:7 - Buku Lopatulika

Onse akudana nane andinong'onezerana; apangana chondiipsa ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Onse akudana nane andinong'onezerana; apangana chondiipsa ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Onse odana nane amanong'onezana za ine, amayesa kuti zoipa zandigwera chifukwa cha kuipa kwanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane, iwo amalingalira zoyipa kwambiri za ine, ponena kuti,

Onani mutuwo



Masalimo 41:7
8 Mawu Ofanana  

Pakuti ndamva ugogodi wa ambiri, mantha andizinga. Pondipangira chiwembu, anatsimikiza mtima kulanda moyo wanga.


Munthu wokhota amautsa makani; kazitape afetsa ubwenzi.


Posowa nkhuni moto ungozima; ndi popanda kazitape makangano angoleka.


Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.


anadzala ndi zosalungama zonse, kuipa, kusirira, dumbo; odzala ndi kaduka, mbanda, ndeu, chinyengo, udani;


Pakuti ndiopa, kuti kaya, pakudza ine, sindidzakupezani inu otere onga ndifuna, ndipo ine ndidzapezedwa ndi inu wotere wonga simufuna; kuti kaya pangakhale chotetana, kaduka, mikwiyo, zilekanitso, maugogodi, ukazitape, zodzikuza, mapokoso;