Mateyu 22:15 - Buku Lopatulika15 Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Nthaŵi ina Afarisi adakapangana zodzatapa Yesu m'kamwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kenaka Afarisi anatuluka nakakonza njira zomupezera zifukwa Yesu mʼmawu ake. Onani mutuwo |