Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:15 - Buku Lopatulika

15 Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Nthaŵi ina Afarisi adakapangana zodzatapa Yesu m'kamwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Kenaka Afarisi anatuluka nakakonza njira zomupezera zifukwa Yesu mʼmawu ake.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:15
14 Mawu Ofanana  

Adzikhazikitsa mafumu a dziko lapansi, nachita upo akulu pamodzi, Kutsutsana naye Yehova, ndi Wodzozedwa wake, ndi kuti,


Ndipo akadza kundiona wina angonena bodza; mumtima mwake adzisonkhera zopanda pake, akanka nayenda namakanena.


Ananditchera ukonde apo ndiyenda; moyo wanga wawerama. Anandikumbira mbuna patsogolo panga; anagwa m'kati mwake iwo okha.


Pakuti onani, alalira moyo wanga; amphamvu andipangira chiwembu, osachimwa, osalakwa ine, Yehova,


amene apalamulitsa munthu mlandu, namtchera msampha iye amene adzudzula pachipata, nambweza wolungama ndi chinthu chachabe.


Ndipo iwo anati, Tiyeni, tilingalire Yeremiya chomchitira choipa; pakuti chilamulo sichidzathera wansembe, kapena uphungu wanzeru, kapena mau mneneri. Tiyeni, timpande iye ndi lilime, tisamvere iye mau ake ali onse.


Pakuti ndamva kugogodera kwa ambiri, mantha pozungulira ponse. Neneza, ndipo tidzamneneza iye, ati atsamwali anga onse, amene ayang'anira kutsimphina kwanga; kapena adzakopedwa, ndipo ife tidzampambana iye, ndipo tidzambwezera chilango.


Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga.


Koma ichi ndinena mwa kupindula kwanu kwa inu nokha; sikuti ndikakutchereni msampha, koma kukuthandizani kuchita chimene chiyenera, ndi kutsata chitsatire Ambuye, opanda chocheukitsa.


Pakuti talingirirani Iye amene adapirira ndi ochimwa otsutsana naye kotere, kuti mungaleme ndi kukomoka m'moyo mwanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa