Mateyu 22:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti oitanidwa ndiwo ambiri, koma osankhidwa ndiwo owerengeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti oitanidwa ndiwo ambiri, koma osankhidwa ndiwo owerengeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono Yesu adati, “Inde oitanidwa ngambiri, komatu osankhidwa ngoŵerengeka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Popeza oyitanidwa ndi ambiri koma osankhidwa ndi ochepa.” Onani mutuwo |