Masalimo 31:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti ndamva ugogodi wa ambiri, mantha andizinga. Pondipangira chiwembu, anatsimikiza mtima kulanda moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti ndamva ugogodi wa ambiri, mantha andizinga. Pondipangira chiwembu, anatsimikiza mtima kulanda moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Zoonadi, ndimamva anthu ambiri akunong'onezana zoipa za ine, zoopsa zandizinga ponseponse. Amapangana zoti andiwukire, namachita upo woipa woti andiphe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti ine ndamva zonena zoyipa za anthu ambiri; zoopsa zandizungulira mbali zonse; iwo akukonza chiwembu kuti alimbane nane, kuti atenge moyo wanga. Onani mutuwo |