Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 41:8 - Buku Lopatulika

8 Chamgwera chinthu choopsa, ati; popeza ali gonire sadzaukanso.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Chamgwera chinthu choopsa, ati; popeza ali gonire sadzaukanso.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Amati, “Yamgwera nthenda yofa nayo, sadzukanso pamene wagonapo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 “Matenda owopsa amugwira; sadzaukapo pamalo pamene wagona.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 41:8
7 Mawu Ofanana  

Ambiri amati kwa moyo wanga, alibe chipulumutso mwa Mulungu.


ndi kuti, Wamsiya Mulungu. Mlondoleni, mgwireni; popeza palibe wompulumutsa.


Ndipo mkazi uyu, ndiye mwana wa Abrahamu, amene Satana anammanga, onani, zaka khumi ndi zisanu ndi zitatu, nanga si kuyenera kodi, kuti amasulidwe nsinga yake imeneyi tsiku la Sabata?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa