Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 148:3 - Buku Lopatulika

Mlemekezeni, dzuwa ndi mwezi; mlemekezeni, nyenyezi zonse zounikira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mlemekezeni, dzuwa ndi mwezi; mlemekezeni, nyenyezi zonse zounikira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtamandeni inu dzuŵa ndi mwezi, mtamandeni inu nonse nyenyezi zoŵala!

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mutamandeni, inu dzuwa ndi mwezi, mutamandeni, inu nonse nyenyezi zowala.

Onani mutuwo



Masalimo 148:3
8 Mawu Ofanana  

Pakukhalabe masiku a dziko lapansi, nthawi yakubzala ndi yakukunkha, chisanu ndi mafundi, malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku sizidzalekai.


Pakuti Yehova atero: Ngati mukhoza kuswa pangano langa la usana ndi pangano langa la usiku, kuti usakhalenso usana ndi usiku, m'nyengo yao;


ndi kuti mungakweze maso anu kupenya kumwamba, ndipo poona dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi, khamu lonse la kumwamba, munganyengedwe ndi kuzigwadira, ndi kuzitumikira, zimene Yehova Mulungu wanu anagawira mitundu yonse ya anthu pansi pa thambo lonse.