Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 146:1 - Buku Lopatulika

Aleluya; Ulemekeze Yehova, moyo wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Aleluya; Ulemekeze Yehova, moyo wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tamandani Chauta! Tamanda Chauta, iwe mtima wanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tamandani Yehova. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

Onani mutuwo



Masalimo 146:1
4 Mawu Ofanana  

Lemekeza Yehova, moyo wanga; ndi zonse za m'kati mwanga zilemekeze dzina lake loyera.


Lemekezani Yehova, inu, ntchito zake zonse, ponseponse pali ufumu wake: Lemekeza Yehova, moyo wanga iwe.


Ochimwa athedwe kudziko lapansi, ndi oipa asakhalenso. Yamika Yehova, moyo wanga. Aleluya.


Kuti asamalire malemba ake, nasunge malamulo ake. Aleluya.