Masalimo 145:21 - Buku Lopatulika21 Pakamwa panga padzanena chilemekezo cha Yehova; ndi zinthu zonse zilemekeze dzina lake loyera kunthawi za nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakamwa panga padzanena chilemekezo cha Yehova; ndi zinthu zonse zilemekeze dzina lake loyera kunthawi za nthawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Pakamwa panga padzayamika Chauta, zamoyo zonse zitamande dzina lake loyera mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pakamwa panga padzayankhula zotamanda Yehova. Cholengedwa chilichonse chitamande dzina lake loyera ku nthawi za nthawi. Onani mutuwo |