Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 146:2 - Buku Lopatulika

2 Ndidzalemekeza Yehova m'moyo mwanga; ndidzaimbira zomlemekeza Mulungu wanga pokhala ndi moyo ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndidzalemekeza Yehova m'moyo mwanga; ndidzaimbira zomlemekeza Mulungu wanga pokhala ndi moyo ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndidzatamanda Chauta pa moyo wanga wonse. Ndidzaimba nyimbo zotamanda Mulungu wanga nthaŵi zonse pamene ndili moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse; ndidzayimba nyimbo zamatamando kwa Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 146:2
6 Mawu Ofanana  

Ndidzaimbira Yehova m'moyo mwanga: ndidzaimbira Mulungu wanga zomlemekeza pokhala ndilipo.


Potero ndidzakuyamikani m'moyo mwanga; ndidzakweza manja anga m'dzina lanu.


Imvani mafumu inu; tcherani makutu, akalonga inu; ndidzamuimbira ine Yehova, inetu; ndidzamuimbira nyimbo, Yehova, Mulungu wa Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa