Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 139:9 - Buku Lopatulika

Ndikadzitengera mapiko a mbandakucha, ndi kukhala ku malekezero a nyanja;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikadzitengera mapiko a mbandakucha, ndi kukhala ku malekezero a nyanja;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikaulukira kotulukira dzuŵa, kapena kukafika kuzambwe, ku mathero a nyanja,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati ndiwulukira kotulukira dzuwa, ngati ndikakhala ku malekezero a nyanja,

Onani mutuwo



Masalimo 139:9
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anaberekeka pa kerubi, nauluka; nauluka msanga pa mapiko a mphepo.


Kutuluka kwake lituluka kolekezera thambo, ndipo kuzungulira kwake lifikira ku malekezero ake; ndipo kulibe kanthu kobisalira kutentha kwake.


Koma inu akuopa dzina langa, dzuwa la chilungamo lidzakutulukirani, muli kuchiritsa m'mapiko mwake; ndipo mudzatuluka ndi kutumphatumpha ngati anaang'ombe onenepa otuluka m'khola.