Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 19:6 - Buku Lopatulika

6 Kutuluka kwake lituluka kolekezera thambo, ndipo kuzungulira kwake lifikira ku malekezero ake; ndipo kulibe kanthu kobisalira kutentha kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Kutuluka kwake lituluka kolekezera thambo, ndipo kuzungulira kwake lifikira ku malekezero ake; ndipo kulibe kanthu kobisalira kutentha kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Limatuluka kuyambira ku mathero ena a thambo, ndi kuzungulira mpaka ku mathero enanso. Palibe chinthu chilichonse chotha kulewa kutentha kwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo ndi kuzungulira mpaka mbali inanso; palibe chinthu chotha kupewa kutentha kwake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 19:6
7 Mawu Ofanana  

Mitambo ndiyo chomphimba, kuti angaone; ndipo amayenda pa thambo lakumwamba.


Ngati awerengedwa makamu ake? Ndipo ndaniyo, kuunika kwake sikumtulukira?


Chitulukire dzuwa kufikira kulowa kwake lilemekezedwe dzina la Yehova.


Ndikadzitengera mapiko a mbandakucha, ndi kukhala ku malekezero a nyanja;


Inde dzuwa lituluka, nililowa, nilifulumira komwe linatulukako.


ngatitu, mukhalabe m'chikhulupiriro, ochilimika ndi okhazikika ndi osasunthika kulekana nacho chiyembekezo cha Uthenga Wabwino umene mudaumva, wolalikidwa cholengedwa chonse cha pansi pa thambo; umene ine Paulo ndakhala mtumiki wake.


Adani anu onse, Yehova, atayike momwemo. Koma iwo akukonda Inu akhale ngati dzuwa lotuluka mu mphamvu yake. Ndipo dziko linapumula zaka makumi anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa