Masalimo 19:7 - Buku Lopatulika7 Malamulo a Yehova ali angwiro, akubwezera moyo; mboni za Yehova zili zokhazikika, zakuwapatsa opusa nzeru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Malamulo a Yehova ali angwiro, akubwezera moyo; mboni za Yehova zili zokhazikika, zakuwapatsa opusa nzeru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mau a Chauta ngangwiro, amapatsa munthu moyo watsopano. Umboni wa Chauta ndi wokhulupirika, umaŵapatsa nzeru amene alibe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Lamulo la Yehova ndi langwiro, kutsitsimutsa moyo. Maumboni a Yehova ndi odalirika, amapereka nzeru kwa wopanda nzeru. Onani mutuwo |