Masalimo 18:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anaberekeka pa kerubi, nauluka; nauluka msanga pa mapiko a mphepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anaberekeka pa kerubi, nauluka; nauluka msanga pa mapiko a mphepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adakwera pa mkerubi nauluka. Adayenda mwaliŵiro ndi mphepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka; nawuluka ndi mphepo mwaliwiro. Onani mutuwo |