Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 132:3 - Buku Lopatulika

Ngati ndidzalowa pakhomo pa nyumba yanga, ngati ndidzakwera pa kama logonapo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ngati ndidzalowa pakhomo pa nyumba yanga, ngati ndidzakwera pa kama logonapo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ndithu sindidzaloŵa m'nyumba mwanga, kapena kukagona pabedi panga,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Sindidzalowa mʼnyumba mwanga kapena kugona pa bedi langa:

Onani mutuwo



Masalimo 132:3
3 Mawu Ofanana  

Chilichonse dzanja lako lichipeza kuchichita, uchichite ndi mphamvu yako; pakuti mulibe ntchito ngakhale kulingirira ngakhale kudziwa, ngakhale nzeru, kumanda ulikupitako.


Kodi imeneyi ndiyo nthawi yakuti inu nokha mukhala m'nyumba zanu zochingidwa m'katimo, ndi nyumba iyi ikhale yopasuka?


Koma muyambe mwafuna Ufumu wake ndi chilungamo chake, ndipo zonse zimenezo zidzaonjezedwa kwa inu.