Mateyu 6:33 - Buku Lopatulika33 Koma muyambe mwafuna Ufumu wake ndi chilungamo chake, ndipo zonse zimenezo zidzaonjezedwa kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Koma muthange mwafuna Ufumu wake ndi chilungamo chake, ndipo zonse zimenezo zidzaonjezedwa kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma inu, yambani mwafunafuna ufumu wa Mulungu ndi kumachita zimene Iye akufuna, ndipo zina zonsezi adzakupatsaninso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma muyambe mwafuna ufumu wake ndi chilungamo chake ndipo zinthu zonsezi zidzapatsidwa kwa inu. Onani mutuwo |