Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 132:4 - Buku Lopatulika

4 ngati ndidzalola maso anga agone, kapena zikope zanga ziodzere;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 ngati ndidzalola maso anga agone, kapena zikope zanga ziodzere;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 sindidzalola kuti ndikhale m'tulo kapena kuti zikope zanga ziwodzere,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 sindidzalola kuti maso anga agone, kapena zikope zanga ziwodzere,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 132:4
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anaika chakudya pamaso pake: koma anati, Sindidzadya ndisananene chimene ndadzera. Ndipo anati, Nenatu.


Usaone tulo m'maso mwako, ngakhale kuodzera zikope zako.


Ndipo anati, Khala ulipo, mwana wanga, mpaka udziwa umo ukhalire mlandu; pakuti munthuyo sadzauleka mpaka atautha mlanduwo lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa