Hagai 1:4 - Buku Lopatulika4 Kodi imeneyi ndiyo nthawi yakuti inu nokha mukhala m'nyumba zanu zochingidwa m'katimo, ndi nyumba iyi ikhale yopasuka? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kodi imeneyi ndiyo nthawi yakuti inu nokha mukhala m'nyumba zanu zochingidwa m'katimo, ndi nyumba iyi ikhale yopasuka? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Kodi nzabwino zimenezi kuti inuyo muzikhala m'nyumba zomanga bwino, pamene Nyumba yangayi ili bwinja? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Kodi ino ndi nthawi yoti inuyo muzikhala mʼnyumba zomanga bwino, pamene Nyumba yangayi ikanali bwinja?” Onani mutuwo |