Masalimo 132:2 - Buku Lopatulika2 Kuti analumbira Yehova, nawindira Wamphamvuyo wa Yakobo, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kuti analumbira Yehova, nawindira Wamphamvuyo wa Yakobo, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adalumbira kwa Inu Chauta, nalonjeza kwa Mulungu Wamphamvuzonse wa Yakobe kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye analumbira kwa Yehova ndi kulonjeza kwa Wamphamvu wa Yakobo kuti, Onani mutuwo |