Taonani, m'mwemo adzadalitsika munthu wakuopa Yehova.
Zoonadi, ndimo m'mene adzakhalire wodala munthu woopa Chauta.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.
Adzadalitsa iwo akuopa Yehova, aang'ono ndi aakulu.
ndipo madalitso awa onse adzakugwerani, ndi kukupezani, mukadzamvera mau a Yehova Mulungu wanu.