Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 128:4 - Buku Lopatulika

Taonani, m'mwemo adzadalitsika munthu wakuopa Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Taonani, m'mwemo adzadalitsika munthu wakuopa Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zoonadi, ndimo m'mene adzakhalire wodala munthu woopa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 128:4
2 Mawu Ofanana  

Adzadalitsa iwo akuopa Yehova, aang'ono ndi aakulu.


ndipo madalitso awa onse adzakugwerani, ndi kukupezani, mukadzamvera mau a Yehova Mulungu wanu.