Masalimo 115:13 - Buku Lopatulika13 Adzadalitsa iwo akuopa Yehova, aang'ono ndi aakulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Adzadalitsa iwo akuopa Yehova, aang'ono ndi aakulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adzadalitsa amene amamlemekeza, anthu wamba ndi apamwamba omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova; aangʼono ndi aakulu omwe. Onani mutuwo |