Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 122:3 - Buku Lopatulika

Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda woundana bwino:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yerusalemu anamangidwa ngati mudzi woundana bwino:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yerusalemu adamangidwa bwino, zigawo zake zonse nzogwirizana pamodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.

Onani mutuwo



Masalimo 122:3
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anakhala m'linga muja, nalitcha mzinda wa Davide. Davide namanga linga pozinga ponse kuyambira ku Milo ndi m'kati momwe.


Koma tinamanga lingali, ndi linga lonse linalumikizana kufikira pakatimpakati; popeza mitima ya anthu inalunjika kuntchito.


Yehova amanga Yerusalemu; asokolotsa otayika a Israele.