Nehemiya 4:6 - Buku Lopatulika6 Koma tinamanga lingali, ndi linga lonse linalumikizana kufikira pakatimpakati; popeza mitima ya anthu inalunjika kuntchito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma tinamanga lingali, ndi linga lonse linalumikizana kufikira pakatimpakati; popeza mitima ya anthu inalunjika kuntchito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Motero tidamangabe khoma, ndipo khoma lonse tidatha kulimanga mpaka theka la msinkhu wake, chifukwa chakuti anthu adaaikapo mtima pa ntchitoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Choncho ife tinamangabe khomalo kufikira lonse litafika theka la msinkhu wake, chifukwa chakuti anthu anagwira ntchitoyo ndi mtima wawo wonse. Onani mutuwo |