Nehemiya 4:5 - Buku Lopatulika5 ndipo musakwirira mphulupulu yao, ndi kulakwa kwao kusafafanizike pamaso panu; pakuti anautsa mkwiyo wanu pamaso pa omanga linga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo musakwirira mphulupulu yao, ndi kulakwa kwao kusafafanizike pamaso panu; pakuti anautsa mkwiyo wanu pamaso pa omanga linga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Musaŵakhululukire cholakwa chao, musafafanize tchimo lao, popeza kuti aputa ukali wanu pamaso pa amisiri omanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Musawakhululukire mphulupulu zawo kapena kufafaniza machimo awo pamaso panu popeza aputa ukali wanu pamaso pa anthu omanga khoma.” Onani mutuwo |