Masalimo 122:4 - Buku Lopatulika4 Kumene akwerako mafuko, ndiwo mafuko a Yehova; akhale mboni ya kwa Israele, Ayamike dzina la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kumene akwerako mafuko, ndiwo mafuko a Yehova; akhale mboni ya kwa Israele, Ayamike dzina la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Kumeneko kumapita mafuko onse, anthu ake a Chauta, monga momwe adalamulira Israele kuti akayamike dzina la Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova. Onani mutuwo |