Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 122:3 - Buku Lopatulika

3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda woundana bwino:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Yerusalemu anamangidwa ngati mudzi woundana bwino:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Yerusalemu adamangidwa bwino, zigawo zake zonse nzogwirizana pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 122:3
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anakhala m'linga muja, nalitcha mzinda wa Davide. Davide namanga linga pozinga ponse kuyambira ku Milo ndi m'kati momwe.


Koma tinamanga lingali, ndi linga lonse linalumikizana kufikira pakatimpakati; popeza mitima ya anthu inalunjika kuntchito.


Yehova amanga Yerusalemu; asokolotsa otayika a Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa