Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 122:2 - Buku Lopatulika

2 Mapazi athu alinkuima m'zipata zanu, Yerusalemu

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Mapazi athu alinkuima m'zipata zanu, Yerusalemu

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mapazi athu akhala akuima m'kati mwa zipata zako, iwe Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 122:2
5 Mawu Ofanana  

Koma ndinasankha Yerusalemu, kuti dzina langa likhale komweko; ndinasankhanso Davide akhale mfumu ya anthu anga Israele.


Lowani kuzipata zake ndi chiyamiko, ndi kumabwalo ake ndi chilemekezo: Myamikeni; lilemekezeni dzina lake.


Apita mwamphamvu naonjezapo mphamvu, aoneka pamaso pa Mulungu mu Ziyoni.


Undiumbire guwa la nsembe ladothi, nundiphere pomwepo nsembe zako zopsereza, ndi nsembe zako zamtendere, nkhosa zako ndi ng'ombe zako; paliponse ndikumbukiritsa anthu dzina langa ndidzakudzera ndi kukudalitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa