Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 12:8 - Buku Lopatulika

Oipa amayenda mozungulirazungulira, potamanda iwo chonyansa mwa ana a anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Oipa amayenda mozungulirazungulira, potamanda iwo chonyansa mwa ana a anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

pakuti anthu oipa amangoyendayenda ponseponse, ndipo anzao amayamikira zochita zao zoipa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo.

Onani mutuwo



Masalimo 12:8
11 Mawu Ofanana  

Ndiwo ana a opusa, inde ana a anthu opanda dzina; anawaingitsa kuwachotsa m'dziko.


Mkulu akamvera chinyengo, atumiki ake onse ali oipa.


Ndi m'malo mwake adzauka munthu woluluka, amene anthu sanampatse ulemu wa ufumu, koma adzafika kachetechete, nadzalanda ufumu ndi mau osyasyalika.


Efuremu azunzika, apsinjika pa mlanduwo; pakuti anafuna mwini wake kutsata lamulolo.


Pakuti asunga malemba a Omuri, ndi ntchito za nyumba ya Ahabu, ndipo mumayenda mu uphungu wao; kuti ndikusandulize bwinja, ndi okhalamo chotsonya; ndipo mudzasenza chitonzo cha anthu anga.