Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 12:7 - Buku Lopatulika

7 Mudzawasunga, Yehova, mudzawatchinjirizira mbadwo uno kunthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Mudzawasunga, Yehova, mudzawatchinjirizira mbadwo uno kunthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Titetezeni, Inu Chauta, titchinjirizeni nthaŵi zonse kwa anthu ameneŵa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 12:7
15 Mawu Ofanana  

kuti muweruze mlandu wa amasiye ndi wokhalira mphanthi, kuti munthu wa padziko lapansi angaonjeze kuopsa.


Mau anu ngoyera ndithu; ndi mtumiki wanu awakonda.


Yehova adzasungira kutuluka kwako ndi kulowa kwako, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse.


Yehova asunga onse akukondana naye; koma oipa onse adzawaononga.


Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu.


Pakuti Mulungu ndani wosati Yehova? Ndipo thanthwe ndani wosati Mulungu wathu?


Kuopa Yehova kuli mbee, kwakukhalabe nthawi zonse; maweruzo a Yehova ali oona, alungama konsekonse.


Pakuti Yehova akonda chiweruzo, ndipo sataya okondedwa ake. Asungika kosatha, koma adzadula mbumba za oipa.


Ndipo Yehova awathandiza, nawalanditsa; awalanditsa kwa oipa nawapulumutsa, chifukwa kuti anamkhulupirira Iye.


Ine Yehova ndiusunga uwo; ndidzauthirira madzi nthawi zonse; ndidzausunga usiku ndi usana, kuti angauipse.


Ndipo iye pakuona ambiri a Afarisi ndi a Asaduki akudza ku ubatizo wake, anati kwa iwo, Obadwa a njoka inu, ndani anakulangizani kuthawa mkwiyo ulinkudza?


Inde akonda mitundu ya anthu; opatulidwa ake onse ali m'dzanja mwanu; ndipo akhala pansi ku mapazi anu; yense adzalandirako mau anu.


amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa chikhulupiriro, kufikira chipulumutso chokonzeka kukavumbulutsidwa nthawi yotsiriza.


Yuda, kapolo wa Yesu Khristu, ndi mbale wa Yakobo, kwa iwo oitanidwa, okondedwa mwa Mulungu Atate, ndi osungidwa ndi Yesu Khristu:


Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa