Masalimo 12:6 - Buku Lopatulika6 Mau a Yehova ndi mau oona; ngati siliva woyenga m'ng'anjo yadothi, yoiyeretsa kasanu ndi kawiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mau a Yehova ndi mau oona; ngati siliva woyenga m'ng'anjo yadothi, yoiyeretsa kasanu ndi kawiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Malonjezo a Chauta ndi angwiro, ali ngati siliva womkometsa m'ng'anjo yamoto, woyeretsedwa kasanunkaŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi, oyengedwa kasanu nʼkawiri. Onani mutuwo |