Masalimo 12:8 - Buku Lopatulika8 Oipa amayenda mozungulirazungulira, potamanda iwo chonyansa mwa ana a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Oipa amayenda mozungulirazungulira, potamanda iwo chonyansa mwa ana a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 pakuti anthu oipa amangoyendayenda ponseponse, ndipo anzao amayamikira zochita zao zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo. Onani mutuwo |