Masalimo 13:1 - Buku Lopatulika1 Mudzandiiwala chiiwalire, Yehova, kufikira liti? Mudzandibisira ine nkhope yanu kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mudzandiiwala chiiwalire, Yehova, kufikira liti? Mudzandibisira ine nkhope yanu kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Kodi mpaka liti, Inu Chauta? Kodi mudzandiiŵala mpaka muyaya? Kodi mudzandibisira nkhope yanu nthaŵi zonse? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu? Onani mutuwo |