Masalimo 13:2 - Buku Lopatulika2 Ndidzachita uphungu m'moyo mwanga kufikira liti, pokhala ndi chisoni m'mtima mwanga tsiku lonse? Adzandiukira ine mdani wanga kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidzachita uphungu m'moyo mwanga kufikira liti, pokhala ndi chisoni m'mtima mwanga tsiku lonse? Adzandiukira ine mdani wanga kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kodi ndizivutika m'maganizo mwanga mpaka liti? Kodi ndiyenera kukhala ndi chisoni mumtima mwanga usana ndi usiku? Kodi mdani wanga azindipambana mpakampaka? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana? Onani mutuwo |