Hoseya 5:11 - Buku Lopatulika11 Efuremu azunzika, apsinjika pa mlanduwo; pakuti anafuna mwini wake kutsata lamulolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Efuremu azunzika, apsinjika pa mlanduwo; pakuti anafuna mwini wake kutsata lamulolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Aefuremu akuŵapondereza, akuŵalanga chifukwa chomvera za ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Efereimu waponderezedwa, akulangidwa chifukwa chotsatira mafano. Onani mutuwo |