Hoseya 5:10 - Buku Lopatulika10 Akalonga a Yuda akunga anthu osuntha malire; ndidzawatsanulira mkwiyo wanga ngati madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Akalonga a Yuda akunga anthu osuntha malire; ndidzawatsanulira mkwiyo wanga ngati madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta akuti, “Atsogoleri a ku Yuda amachita nkhondo kuti afutuze malire. Nchifukwa chake ndidzaŵamiza ndi mkwiyo wanga ngati madzi achigumula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Atsogoleri a Yuda ali ngati anthu amene amasuntha miyala ya mʼmalire. Ndidzawakhutulira ukali wanga ngati madzi a chigumula. Onani mutuwo |