Hoseya 5:9 - Buku Lopatulika9 Efuremu adzasanduka bwinja tsiku lakudzudzula; mwa mafuko a Israele ndadziwitsa chodzachitikadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Efuremu adzasanduka bwinja tsiku lakudzudzula; mwa mafuko a Israele ndadziwitsa chodzachitikadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Efuremu adzasanduka bwinja pa tsiku lachilango. Ndikulengeza zoona kwa inu nonse Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Efereimu adzasanduka bwinja pa tsiku la chilango. Ine ndikulengeza zomwe zidzachitikadi pakati pa mafuko a Israeli. Onani mutuwo |