Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:3 - Buku Lopatulika

Anene tsono nyumba ya Aroni, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anene tsono nyumba ya Aroni, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Banja la Aroni linene kuti, “Chikondi chake nchamuyaya.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Banja la Aaroni linene kuti, “Chikondi chake ndi chosatha.”

Onani mutuwo



Masalimo 118:3
6 Mawu Ofanana  

Nyumba ya Aroni, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao, ndi chikopa chao.


inunso ngati miyala yamoyo mumangidwa nyumba ya uzimu, kuti mukhale ansembe oyera mtima, akupereka nsembe zauzimu, zolandiridwa ndi Mulungu mwa Yesu Khristu.


natiyesa ife ufumu tikhale ansembe a Mulungu ndiye Atate wake; kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu kufikira nthawi za nthawi. Amen.