Masalimo 115:10 - Buku Lopatulika10 Nyumba ya Aroni, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao, ndi chikopa chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Nyumba ya Aroni, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao, ndi chikopa chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Iwe banja la Aroni khulupirira Chauta. Chauta ndiye mthandizi wako ndi chishango chako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova; Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako. Onani mutuwo |