Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:12 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwanenedwa, Usamuyese Ambuye Mulungu wako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwanenedwa, Usamuyese Ambuye Mulungu wako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Yesu adati, “Malembo akuti, ‘Usaŵayese Ambuye, Mulungu wako.’ ”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anayankha kuti, “Mawu akuti, ‘Musamuyese Yehova Mulungu wanu.’ ”

Onani mutuwo



Luka 4:12
8 Mawu Ofanana  

Popeza analakalakatu kuchidikhako, nayesa Mulungu m'chipululu.


Pamene makolo anu anandisuntha, anandiyesa, anapenyanso chochita Ine.


Ndipo tsopano tiwatcha odzikuza odala, inde iwo ochita zoipa amangidwa ngati nyumba; inde, ayesa Mulungu, napulumuka.


Yesu ananena naye, Ndiponso kwalembedwa, Usamuyese Ambuye Mulungu wako.


Ndipo mdierekezi, m'mene adamaliza mayesero onse, analekana naye kufikira nthawi ina.


Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija.


Musamayesa Yehova Mulungu wanu, monga munamyesa mu Masa.