Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo mdierekezi, m'mene adamaliza mayesero onse, analekana naye kufikira nthawi ina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo mdierekezi, m'mene adamaliza mayesero onse, analekana naye kufikira nthawi ina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Tsono Satana atatha kumuyesa mwa zonsezi, adalekana naye, kudikira nthaŵi ina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mdierekezi atamaliza mayesero awa onse, anamusiya Iye kufikira atapeza mpata wina.

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:13
6 Mawu Ofanana  

Pomwepo mdierekezi anamsiya Iye, ndipo onani, angelo anadza, namtumikira Iye.


Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwanenedwa, Usamuyese Ambuye Mulungu wako.


Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.


Sindidzalankhulanso zambiri ndi inu, pakuti mkulu wa dziko lapansi adza; ndipo alibe kanthu mwa Ine;


Pakuti sitili naye mkulu wa ansembe wosatha kumva chifundo ndi zofooka zathu; koma wayesedwa m'zonse monga momwe ife, koma wopanda uchimo.


Potero mverani Mulungu; koma kanizani mdierekezi, ndipo adzakuthawani inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa