Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo, Pa manja ao adzakunyamula iwe, kuti ungagunde konse phazi lako pamwala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo, Pa manja ao adzakunyamula iwe, kuti ungagunde konse phazi lako pamwala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 “ ‘Iwo adzakunyamulani m'manja mwao, kuti mapazi anu angapweteke pa miyala.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 ndipo adzakunyamula ndi manja awo, kuti phazi lako lisagunde pa mwala.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:11
3 Mawu Ofanana  

Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, akusunge m'njira zako zonse.


Adzakunyamula pa manja ao, ungagunde phazi lako pamwala.


nanena naye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, mudzigwetse nokha pansi: pakuti kwalembedwa, kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, ndipo pa manja ao adzakunyamula iwe, ungagunde konse phazi lako pamwala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa