Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:10 - Buku Lopatulika

10 pakuti kwalembedwa kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, kuti akutchinjirize.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 pakuti kwalembedwa kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, kuti akutchinjirize.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Paja Malembo akuti, “ ‘Mulungu adzalamula angelo ake kuti akusamaleni.’ Ndiponso,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Pakuti kwalembedwa, “Adzalamulira angelo ake za iwe kuti akutchinjirize mosamala;

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo, Pa manja ao adzakunyamula iwe, kuti ungagunde konse phazi lako pamwala.


Ndipo mdierekezi anati kwa Iye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, uzani mwala uwu usanduke mkate.


Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwalembedwa, kuti, Ambuye Mulungu wako uzimgwadira, ndipo Iye yekhayekha uzimtumikira.


Ndipo kulibe kudabwa; pakuti Satana yemwe adzionetsa ngati mngelo wa kuunika.


Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa