Masalimo 95:9 - Buku Lopatulika9 Pamene makolo anu anandisuntha, anandiyesa, anapenyanso chochita Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamene makolo anu anandisuntha, anandiyesa, anapenyanso chochita Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 pamene makolo anu adandiputa mondiyesa ngakhale anali ataona ntchito zanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kumene makolo anu anandiyesa ndi kundiputa, ngakhale anaona zimene Ine ndinazichita. Onani mutuwo |