Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:3 - Buku Lopatulika

Ndipo onse anamuka kulembedwa, munthu aliyense kumzinda wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo onse anamuka kulembedwa, munthu aliyense kumudzi wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero anthu onse adapita kukalembedwa, aliyense ku mudzi kwao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo aliyense anapita ku mzinda wa kwawo kukalembetsa.

Onani mutuwo



Luka 2:3
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Efuroni anakhala pakati pa ana a Hiti, ndipo Efuroni Muhiti anayankha Abrahamu alinkumva ana a Hiti, onse amene analowa pa chipata cha mzinda wake, kuti,


Ndipo kunali masiku aja, kuti lamulo linatuluka kwa Kaisara Augusto kuti dziko lonse lokhalamo anthu lilembedwe;


ndiko kulembera koyamba pokhala Kwirinio kazembe wa Siriya.


Ndipo Yosefe yemwe anakwera kuchokera ku Galileya, kumzinda wa Nazarete, kunka ku Yudeya, kumzinda wa Davide, dzina lake Betelehemu, chifukwa iye anali wa banja ndi fuko lake la Davide;


kukalembedwa iye mwini pamodzi ndi Maria, wopalidwa naye ubwenzi; ndi uyu anali ndi pakati.