Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 2:5 - Buku Lopatulika

5 kukalembedwa iye mwini pamodzi ndi Maria, wopalidwa naye ubwenzi; ndi uyu anali ndi pakati.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 kukalembedwa iye mwini pamodzi ndi Maria, wopalidwa naye ubwenzi; ndi uyu anali ndi pakati.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Adapita kukalembedwa pamodzi ndi Maria, mkazi wake, amene anali ndi pathupi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Iye anapita kumeneko kukalembetsa pamodzi ndi Mariya, amene anapalana naye ubwenzi kuti akwatirane ndipo anali woyembekezera.

Onani mutuwo Koperani




Luka 2:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali masiku aja, kuti lamulo linatuluka kwa Kaisara Augusto kuti dziko lonse lokhalamo anthu lilembedwe;


Ndipo onse anamuka kulembedwa, munthu aliyense kumzinda wake.


Ndipo Yosefe yemwe anakwera kuchokera ku Galileya, kumzinda wa Nazarete, kunka ku Yudeya, kumzinda wa Davide, dzina lake Betelehemu, chifukwa iye anali wa banja ndi fuko lake la Davide;


Ndipo panali pokhala iwo komweko, masiku ake a kubala anakwanira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa