Luka 2:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo panali pokhala iwo komweko, masiku ake a kubala anakwanira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo panali pokhala iwo komweko, masiku ake a kubala anakwanira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene anali kumeneko, nthaŵi yake yoti Maria achire idakwana, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ali kumeneko, nthawi inakwana yakuti mwana abadwe, Onani mutuwo |