Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 8:3 - Buku Lopatulika

ndipo madzi anaphweraphwerabe padziko lapansi: pamene anatha masiku zana limodzi kudza makumi atatu madzi anachepa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo madzi anaphweraphwerabe pa dziko lapansi: pamene anatha masiku zana limodzi kudza makumi atatu madzi anachepa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo madzi adayamba kutsika pang'onopang'ono. Masiku 150 atapita, madziwo anali atatsika ndithu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Madzi amaphwabe pa dziko lapansi. Pakutha pa masiku 150, madzi anatsika,

Onani mutuwo



Genesis 8:3
3 Mawu Ofanana  

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.


Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.


Ndipo madzi analinkuchepa kufikira mwezi wakhumi; mwezi wakhumi tsiku loyamba mwezi ndipo padaoneka mitu ya mapiri.