Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 7:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Madziwo adakhala osaphwa konse pa dziko lapansi masiku 150.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 7:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anakumbukira Nowa ndi zamoyo zonse, ndi nyama zonse zimene zinali pamodzi naye m'chingalawamo; ndipo Mulungu anapititsa mphepo padziko lapansi, naphwa madzi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa