Genesis 8:2 - Buku Lopatulika2 ndipo anatsekedwa akasupe a madzi aakulu ndi mazenera a kumwamba, niletsedwa mvula ya kumwamba; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo anatsekedwa akasupe a madzi aakulu ndi mazenera a kumwamba, niletsedwa mvula ya kumwamba; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Akasupe a madzi ambiri okhala pansi pa dziko pamodzi ndi zipata zakuthambo, adazitseka. Mvula adailetsa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsono akasupe a madzi ambiri a pansi pa dziko ndi zitseko za madzi a kumwamba zinatsekedwa, ndipo mvula inaleka kugwa. Onani mutuwo |