Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 7:18 - Buku Lopatulika

Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu padziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu pa dziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Madziwo adanka nakwererakwerera, ndipo chombocho chidayandama pa madzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Madzi anafika mwamphamvu ndipo anachulukirachulukira pa dziko lapansi moti chombo chinayandama pamwamba pa madziwo.

Onani mutuwo



Genesis 7:18
6 Mawu Ofanana  

Ndipo chigumula chinali padziko lapansi masiku makumi anai: ndipo madzi anachuluka natukula chingalawa, ndipo chinakwera pamwamba padziko lapansi.


Ndipo madzi anapambana ndithu padziko lapansi; anamizidwa mapiri aatali onse amene anali pansi pathambo lonse.


Amene anakwatulidwa isanafike nyengo yao, chigumula chinakokolola kuzika kwao;


M'mwemo muyenda zombo; ndi Leviyatani amene munamlenga aseweremo.


Chigumula chisandifotsere, ndipo chakuya chisandimize; ndipo asanditsekere pakamwa pake pa dzenje.


Popeza madziwo anabwerera, namiza magaleta ndi apakavalo, ndiwo nkhondo yonse ya Farao imene idalowa pambuyo pao m'nyanja; sanatsale wa iwowa ndi mmodzi yense.