Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 104:26 - Buku Lopatulika

26 M'mwemo muyenda zombo; ndi Leviyatani amene munamlenga aseweremo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 M'mwemo muyenda zombo; ndi Leviyatani amene munamlenga aseweremo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Zombo zimayendamo pamodzi ndi Leviyatani, chilombo chija chimene mudachilenga kuti chiziseŵera m'madzimo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Kumeneko sitima zapamadzi zimayenda uku ndi uku, ndiponso Leviyatani amene munamulenga kuti asewere kumeneko.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:26
8 Mawu Ofanana  

Zebuloni adzakhala m'mphepete mwa nyanja; ndipo iye adzakhala dooko la ngalawa; ndipo malire ake adakhala pa Sidoni.


Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu padziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi.


Autemberere iwo akutemberera usana, Odziwa kuutsa Leviyatani.


Iwo akutsikira kunyanja nalowa m'zombo, akuchita ntchito zao pamadzi aakulu.


Mudaphwanya mitu ya Leviyatani; mudampereka akhale chakudya cha zilombo za m'chipululu.


Tsiku limenelo Yehova ndi lupanga lake lolimba ndi lalikulu ndi lamphamvu adzalanga Leviyatani njoka yothamanga, ndi Leviyatani njoka yopindikapindika; nadzapha ching'ona chimene chili m'nyanja.


Akulu a ku Gebala ndi eni luso ake anali mwa iwe kukonza ziboo zako; zombo zonse za kunyanja pamodzi ndi amalinyero ao anali mwa iwe kusinthana nawe malonda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa